Chichewa:
Tigwirane manja, tigwirizane
Adani athu onse adzagwa pamapazi athu
Chomwe timange padziko
Chidzamangidwa kumwamba
Mu Dzina la Yesu satana adzathawa
Chorus:
Poti tiri ndi mphamvu mu Dzina la Yesu
Ee tiri ndi mphamvu mu dzina la Ambuye
Ngakhale satana akwiye
Sitingagonjetsedwebe
Poti tiri ndi mphamvu mu Dzina la Ambuye
Kwa zaka zambirino, satana wati atilepheletse
Koma Mkwatibwi wa Yesu, Mbuye ali ndi moyobe
Monga asirikali amphamvu, tingoguba cha mtsogolo
Kugonjetsa nkhondo zonse
Poti Ambuye ali mbali yathu!
English:
Give me your hand, let’s agree together
Then all of our enemies will crumble at our feet
For whatever we bind on earth
Shall be bound in Heaven
At the Name of Jesus, satan has to flee
Chorus:
‘Cause we’ve got the power in the Name of Jesus
Yes we’ve got the power in the Name of the Lord
Though satan rages we cannot be defeated
‘Cause we’ve got the power in the Name of the Lord
For many years now satan has tried to stop us
But the Bride of Jesus, Lord, we’re still alive
Like a mighty Army we’ll keep marching onward
Winning every battle, ‘cause the Lord’s on our side!
This is the Chichewa version
Cheers!
Amen!
ReplyDeleteAmen 😊
Delete